nya-x-nyanja_gen_text_reg/30/27.txt

1 line
254 B
Plaintext

\v 27 Labani anamu uza kuti, "Ngati apa uzani chitila chifundo mwamene uvionela vintu, uyembekeze, chifukwa nina ziba mumatesnga kuti Yawe anidalisa ine chifukwa cha iwe." \v 28 Pamene apo anakamba kuti, "kamba mutengo wako weka, ndipo ine nizabalipila."