nya-x-nyanja_gen_text_reg/43/06.txt

1 line
371 B
Plaintext

\v 6 Israeli anakamba, " Chifukwa chani mwani chitila choipa pa kuniuza nyu munthu kuti mulina mubale wanu wina?" \v 7 Bana kamba, " Uyu munthu anati fusa mopitilila zaise ndi banja lathu, ana kamba,' batate banu balimoyo? Kodi muli na mubale wanu wina?' Tina mu yankha eve kulingana ndi mafuso yake. Sembe tina ziba bwanji zamene aza kamba, 'muletani mubale wanu pasi?'"