nya-x-nyanja_gen_text_reg/19/26.txt

1 line
292 B
Plaintext

\v 26 Ndipo mukazi wa Loti, anali kumbuyo kwake, anayangana kumbuyo, ana sanduka cuulu cha saulti. \v 27 Abrahamu ananyamuka kuseni, no yenda pa malo pamene enze anayimilila ana Yehova. \v 28 Anayanga pansi ku Sodoma na Gomora nowona, chusi chinyamuka kuchioka pansi monga chusi chamu fanasi.