Tue Dec 08 2020 12:38:23 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2020-12-08 12:38:23 +02:00
parent dafc1f5e06
commit b04b5879cb
11 changed files with 11 additions and 55 deletions

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\c 29 \v 1 Pamene apo Yakobo anayenda paulendo wake na kufika ku malo ya bantu ba ku maba. \v 2 Pamene anayangana, anaona chisime mumunda, na, onani, magulu yatatu ya mbelele yanali gone mumbali. chifukwa cikuchoka mu chicime ichi banali kumwesalamo mbelele, na mwala unali pakamwa pachisime unali ukulu. \v 3 Pamene yonse magulu mbelele yanakumana paja, na bachibeta banali kuchosa mwala pakamwa pachisime na kupasa mbelele manzi, naku bwezapo chimwala futi pakamw pachisime, nakuchibweza mumalo yake.
=======
\c 29 \v 1 Pamene apo Yakobo ana yenda paulendo wake na kufika ku malo ya banthu ba ku maba. \v 2 Pamene yangana na ana ona cisime mumunda, ndipo onani, mangula yatatu ya mbelele yanali gone mumbali. Chifukwa nikuchoka mu chibelele, Ndipo mwala unali pakamwa kachi cine wenzeli ukuti. \v 3 Pamene yonse Malungu ya mbelele yana kumana paja, na bachibeta banali kuchosa mwala pakamwa kacisime na kupasa mbelele manzi, naku bwezapo chimwala futi pakamwa kacisime, nakuchibweza mu malo mwake.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\c 29 \v 1 Pamene apo Yakobo anayenda paulendo wake na kufika ku malo ya bantu ba ku maba. \v 2 Pamene anayangana, anaona chisime mumunda, na, onani, magulu yatatu ya mbelele yanali gone mumbali. chifukwa cikuchoka mu chicime ichi banali kumwesalamo mbelele, na mwala unali pakamwa pachisime unali ukulu. \v 3 Pamene yonse magulu mbelele yanakumana paja, na bachibeta banali kuchosa mwala pakamwa pachisime na kupasa mbelele manzi, naku bwezapo chimwala futi pakamw pachisime, nakuchibweza mumalo yake.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 4 Yakobo anakamba kuli benve kuti, "ba bale banga, mwachokela kuti?' bana yanka, "Tachokela ku Haran." Anakamba kuli benve, \v 5 "Mumuziba Labani mwana mwamuna wa Naha? "Nabenve banakamba kuti, "Timuziba. " \v 6 anakamba kuli benve kuti, "mwati alibwino?" Benve banakamba kuti, " alichabe bwino, na, yangananei kuja, Recho mwana wake mukazi abwela na mbelele."
=======
\v 4 Yakobo ana kamba kuli beve, "ba bale banga, mwa chokela kuti?" Bana yanka "Ta chokela ku Halan." \v 5 Ana kamba kuli beve, "Mumuziba Labani mwana mwamuna wa Naha?"Nabeve banakamba kuti, "Timuziba." \v 6 Anabakamba kuli beve kuti, "alibwino?" Beve banakamba kuti alibwino, ndipo yanganani kuja, Tacho mwana wake mukazi abwela na mbelele."
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 4 Yakobo anakamba kuli benve kuti, "ba bale banga, mwachokela kuti?' bana yanka, "Tachokela ku Haran." Anakamba kuli benve, \v 5 "Mumuziba Labani mwana mwamuna wa Naha? "Nabenve banakamba kuti, "Timuziba. " \v 6 anakamba kuli benve kuti, "mwati alibwino?" Benve banakamba kuti, " alichabe bwino, na, yangananei kuja, Recho mwana wake mukazi abwela na mbelele."

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 7 Yakobo anakamba, "Onani, ni pakati pa siku. sintawi yama guli ya mbelele kukumana pamozi. mufunika kupasa mbelele manzi na kuyenda na kuzileka zidye." \v 8 Banakamba kuti, "sitinga zipase manzi mpaka zonse mbelele zikumane pamozi. Na bamuna baza chosa chimwala pachisime kuchoka apo tizazipasa manzi mbelele."
=======
\v 7 Yakobo anakamba, "onani, ni pakati pa siku. Sintawi yama gulu ya mbelele kukumana pamodzi. Mufunika kupasa mbelele manzi na kuyenda na kuzilaka zidye. \v 8 Bana kamba kuti, "Sitinga zipase manzi mpaka zonse mbelele zukumana pamozi. na bamuna bazachosa chimwala pakamwa ka chisime ndipo tizazipasa manzi mbelele."
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 7 Yakobo anakamba, "Onani, ni pakati pa siku. sintawi yama guli ya mbelele kukumana pamozi. mufunika kupasa mbelele manzi na kuyenda na kuzileka zidye." \v 8 Banakamba kuti, "sitinga zipase manzi mpaka zonse mbelele zikumane pamozi. Na bamuna baza chosa chimwala pachisime kuchoka apo tizazipasa manzi mbelele."

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 9 Pamene Yakobo anali kukamba na benve, Recho ana bwela na mbelele zaba tate bake, chifukwa niwamene anali kuzibetela. \v 10 Pamene Yakobo anaona recho, mwana mukazi wa Labani, mubale wa bamai bake, na mbelele za Labani, mubale wa bamai bake, Yakobo ana bwela pamene paja, naku vendesa mwala kuchoka pakamwa pachisimenakupasa manzi gulu ya mbelele za Labani, mubale wa bamai bake.
=======
\v 9 Pamene Yakobo anali kukamba na beve, Racho ana bwela na mbelele zaba tate bake, chifukwa mwane anali kuzibetela. \v 10 Pamene Yokobo anaona Racho, mwna mukazi wa Labani, mubale wa bamai bake na mbelele za Labani mubale wa ba mai bake, Yakobo ana bwela pamene paja naku vendesa mwala kuchoka pakamwa kachisime kanupasa manzi gulu ya mbelele za Labani, mubale wa bamai bake.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 9 Pamene Yakobo anali kukamba na benve, Recho ana bwela na mbelele zaba tate bake, chifukwa niwamene anali kuzibetela. \v 10 Pamene Yakobo anaona recho, mwana mukazi wa Labani, mubale wa bamai bake, na mbelele za Labani, mubale wa bamai bake, Yakobo ana bwela pamene paja, naku vendesa mwala kuchoka pakamwa pachisimenakupasa manzi gulu ya mbelele za Labani, mubale wa bamai bake.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 11 Yakobo ana pyopyonta Recho nakulila mo kuwa. Yakobo anauza Recho, kuti enve anali bululu wa batate bake, anali mwana wa Rabeka. \v 12 Pamene apo enve anatmnaga na kuyenda ku'uza batate bake.
=======
\v 11 Yakobo ana pyopyonta Racho nakulila mo kuwa. \v 12 Yakobo ana uza Racho, kuti, eve anali bululu wa ba tate bake, anali mwana mwamuna wa Rebeka.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 11 Yakobo ana pyopyonta Recho nakulila mo kuwa. Yakobo anauza Recho, kuti enve anali bululu wa batate bake, anali mwana wa Rabeka. \v 12 Pamene apo enve anatmnaga na kuyenda ku'uza batate bake.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 13 Pamene Labani ananvela iyi nkani ya Yakobo mwana mwamuna wamulonosi wake, anatamanga kuti bakumane na enve, na kumukumbatila, na kumu pyopyonta, na kumu bwelesa ku nyumba yake. Yakobo anauza Labani vonse ivi vintu. \v 14 Labani ana kamba kuli enve, "iwe zo'ona ndiwe fupa yanga na munofu wanga." ndiye pamene Yakobo ana nkala na paka ntawi ya mwezi umozi.
=======
\v 13 Pamene apo eve anatamanga nakuyenda ku uza ba tate bake. \v 14 Labani ana kamba kuli eve, "Iwe zoona indwe fupa yanga na munofu wanga." Ndeye pamene Yakobo ana nkala na paka ntawi ka mwezi umodzi.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 13 Pamene Labani ananvela iyi nkani ya Yakobo mwana mwamuna wamulonosi wake, anatamanga kuti bakumane na enve, na kumukumbatila, na kumu pyopyonta, na kumu bwelesa ku nyumba yake. Yakobo anauza Labani vonse ivi vintu. \v 14 Labani ana kamba kuli enve, "iwe zo'ona ndiwe fupa yanga na munofu wanga." ndiye pamene Yakobo ana nkala na paka ntawi ya mwezi umozi.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 15 Ndiye pamene Labani anakamba kuli Yakobo kuti unga ni sebenzele mahala chifukwa ndiwe bululu wanga? Niuze, malipilo yako yazankala bwanji?" \v 16 Manje Labani enzeli na bana bakazi bali. Na zina ya mukulu yenze Leya, na zina ya mungono yenze Recho. \v 17 Menso ya Leya yanali yofewa, koma Recho anali okongola, mukapangidwa nama onekedwe. \v 18 Yakobo anakonda Recho, ndiye chamene anakambila, "nizaku sebenzelani zaka seveni ya Recho, mwana wanu mun'gono mukazi.
=======
\v 15 Ndiye pamene Labani anakamba kuli eve, "unga sebezele mahala chifukwa ndewe bululu wanga? niuze malipilo yako yazankhala bwanji?" \v 16 Manje Labani anali na bana bakazi na zina ya mungono yenze Racho. \v 17 Menso ya Leya yanili yafewa, koma Racho anali akongola, mukapangidwe nama onekedwe. \v 18 Yakobo anakonda Racho , ndiye chamene anakamba, "Nizaku sebenzelani zaka seveni ya Racho, mwana wanu mungono mukazi."
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 15 Ndiye pamene Labani anakamba kuli Yakobo kuti unga ni sebenzele mahala chifukwa ndiwe bululu wanga? Niuze, malipilo yako yazankala bwanji?" \v 16 Manje Labani enzeli na bana bakazi bali. Na zina ya mukulu yenze Leya, na zina ya mungono yenze Recho. \v 17 Menso ya Leya yanali yofewa, koma Recho anali okongola, mukapangidwa nama onekedwe. \v 18 Yakobo anakonda Recho, ndiye chamene anakambila, "nizaku sebenzelani zaka seveni ya Recho, mwana wanu mun'gono mukazi.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 19 Labani anakamba kuti, "nicha bwino kuti ine nipupase enve kuli iwe, osati ine nipase enve kuli mwamuna wina. nkala na ine." \v 20 Na Yacobo anasebenza zaka seveni ya Recho; koma yanamuonekela kwati nimasiku yangono, chifukwa cha mwanen ana mukondela.
=======
\v 19 Labani anakamba, "nichabwino kuti ine nimupase eve kuli ewe, osati ine nipase eve kuli mwamuna wina. Nkala na ine." \v 20 Na yakobo anasebeza zaka seveni ya Racho; ndipo kuli eve yana oneka masiku yangono chifukwa cha mwamene ana mukondela.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 19 Labani anakamba kuti, "nicha bwino kuti ine nipupase enve kuli iwe, osati ine nipase enve kuli mwamuna wina. nkala na ine." \v 20 Na Yacobo anasebenza zaka seveni ya Recho; koma yanamuonekela kwati nimasiku yangono, chifukwa cha mwanen ana mukondela.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 21 Pamene apo Yakobo anakamba kuli Labani, "nipase ine mukazi wanga, chifukwa masiku yanga yakwanila kuti nimukwatile!" \v 22 Manje Labani anaitana pamozi bantu bonse ba pamalo nokupanga pwando.
=======
\v 21 Pamene apo Yakobo anakamba kuli Labani, "Nipase ine mukazi wanga, chifukwa masiku yanga yakwanila kuti nimukwatile! \v 22 Manje Labani anaitana pamozi banthu bonse ba pamalo nokupanga pwando.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 21 Pamene apo Yakobo anakamba kuli Labani, "nipase ine mukazi wanga, chifukwa masiku yanga yakwanila kuti nimukwatile!" \v 22 Manje Labani anaitana pamozi bantu bonse ba pamalo nokupanga pwando.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 24 \v 25 \v 26 Yosefe anauza babale bake kuti, "Ine nili pafupi kufa; koma Mulungu azakabwela nafuti kuli imwe naku kusogolelani kuyenda ku ziko yamene analonjeza Abrahamu, na Isaki, nakuli Yakobo."
=======
\v 24 Yosefe ana kamba kwa abale bake, "Nalipa fupi kufa, koma Mulungu zoona azabwela kwa imwe na kuku sogolelani kuku chosa mu malo yamene ana lapa ku pasa Abramu kwa Isaki ndi Yakobo. \v 25 Ndipo Yosefe ana panga bana ba muna ba Israeli kulapila pangano, "Mulungu chazoona aza bwela kwa inu. Patiwe ija mufunika muka yamule ma boza yanga kuyta chosa muno." \v 26 Sopano Yosefe anafa, na zaka 110 bana koza tupi yake ndi po ana ika mu bokosi ku Egipito.
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
\v 24 Yosefe ana kamba kwa abale bake, "Nalipa fupi kufa, koma Mulungu zoona azabwela kwa imwe na kuku sogolelani kuku chosa mu malo yamene ana lapa ku pasa Abramu kwa Isaki ndi Yakobo. \v 25 Ndipo Yosefe ana panga bana ba muna ba Israeli kulapila pangano, "Mulungu chazoona aza bwela kwa inu. Patiwe ija mufunika muka yamule ma boza yanga kuyta chosa muno." \v 26 Sopano Yosefe anafa, na zaka 110 bana koza tupi yake ndi po ana ika mu bokosi ku Egipito.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
Exodus
=======
Mutu 50
>>>>>>> 4d8933d75c6fd9ffd7f088fdef6fdd833ee746b6
Mutu 50