nya-x-nyanja_deu_text_reg/01/29.txt

1 line
407 B
Plaintext

\v 29 Ndipo ninakamba kuli imwe, 'Musankale na manta, kapena musayope beve. \v 30 Yehova Mulungu wanu, wamene ayenda pasogolo panu, azakumenyelani, monga vilivonse vamene anachita kuli imwe mu Igupto pamenso panu, \v 31 na futi muchipululu, kwamene munaona mwamene Yehova Mulungu wanu anakutengelani, monga mwamuna atengela mwana wake mwamuna, kulikonse kwamene munayenda kufikila munabwela kuli yano malo.'