1 line
431 B
Plaintext
1 line
431 B
Plaintext
\c 15 \v 1 Pa kusila kwa zaka zili seveni, mufunika kuchosapo nkongole. \v 2 Iyi ndiye njila kuomboledwa: Aliyense wankongile azachosapo chija chamene anabweleka kuli munzake wapafupi; sazafunsa kuchokela kuli munzake wapafupi kapena mubale wake chifukwa kuchosapo kwa nkongole kwa Yehova kwa kambidwa. \v 3 Kuchokela kuli mulendo mungafunsepo; koma chilichonse cha imwe ngati chili na mubale wanu kwanja kwanu kufunika kulekelako. |