nya-x-nyanja_deu_text_reg/13/06.txt

1 line
493 B
Plaintext

\v 6 Nanga ngati mubale wako, mwana mwamuna wa amai bako, kapena mwana wako mwamuna, kapena mwana wako mukazi, kapena mukazi wako wapachifuba, kapena munzako wamene ali kuli iwe monga umoyo wako, mobisika akakunyengelela iwe nakuti, 'Tiye ndipo tilambile milungu inangu yamene siunazibe, kapena iwe kapena makolo bako- \v 7 iliyonse milungu ya banthu yamene yokuzungulilani, pafupi naimwe, kapena patali naimwe, kuchoka kumozi kosilizila ziko lapansi na kufika kwina kosilizila ziko yapansi.'