nya-x-nyanja_deu_text_reg/01/26.txt

1 line
525 B
Plaintext

\v 26 Koma munakana kuukila, koma muna pandukila mosusana na malamulo ya Yehoha Mulungu wanu. \v 27 Munadandaula mu misasa yanu na kuti, ''Ni chifukwa kuti Yehova anatizonda ife kuti Iye abwelesa kwife kuchoka mu malo ya Igupto, kutipasa mukati mumanja ya Amori kutiononga ife. \v 28 Nikuti kwamene tinga yende manje? Bathu babale bapanga yathu mitima kusungunika, kuti, 'Awo bathu ni bakulu na batali kuchila mwamene tilili; Minzi yawo ni ikulu ndipo niyolimba kufika kumwamba; koma, tababona bana bamuna ba Anakimu kuja.''