nya-x-nyanja_deu_text_reg/01/26.txt

6 lines
1.1 KiB
Plaintext

<<<<<<< HEAD
\v 26 Koma munakana kuukila, koma muna pandukila mosusana na malamulo ya Yehoha Mulungu wanu. \v 27 Munadandaula mu misasa yanu na kuti, ''Ni chifukwa kuti Yehova anatizonda ife kuti Iye abwelesa kwife kuchoka mu malo ya Igupto, kutipasa mukati mumanja ya Amori kutiononga ife. \v 28 Nikuti kwamene tinga yende manje? Bathu babale bapanga yathu mitima kusungunika, kuti, 'Awo bathu ni bakulu na batali kuchila mwamene tilili; Minzi yawo ni ikulu ndipo niyolimba kufika kumwamba; koma, tababona bana bamuna ba Anakimu kuja.''
=======
\v 26 Koma munakana kumenya nkondo, koma munakangana nama lamulo ya Yehova mulungu wanu. \v 27 Munadandaula muma hema yanu nakukamba, '' Nichifukwa chakuti Yehova anatizonda ife nakuti anatichosa mu malo ya Iguputo, kuti pasa mumalo ya baku Amori kuti bati ononge. \v 28 Tizayenda kuti manje? Babale batu balengesa mitima yatu kusungunuka, bakamba, ' Baja bantu nibakulu ndipo nibatali kuchila mwamene tilili; Mizinda yao ni ikulu ndipo ni itali kufika mumwamba; elo, tinaona bana bamuna ba Anakimu kuja.'''
>>>>>>> 31f2266056f1a583193e6f4b2d0ffec4c1748c84