nya-x-nyanja_deu_text_reg/18/17.txt

1 line
316 B
Plaintext

\v 17 Yehova anakamba naine, 'Vamene bakamba vili bwino. \v 18 Nizanyamula muneneli wawo kuchoka muli mubale wawo, monga chabe iwe. Nizaika mau yanga mukamwa kake, ndipo azakamba kuli beve vonse vamene nizamuuza. \v 19 Chizachitika ngati aliyense sazanvela ku mau yanga kuti akamba muzina yanga, nizayafuna kuli eve.