nya-x-nyanja_deu_text_reg/18/20.txt

1 line
295 B
Plaintext

\v 20 Koma muneneli wamene akamba mau mozikuza muzina yanga, mau yamene sininamulile kuti akambe, kapena wamene akamba muzina ya milungu inangu, wamene uyo muneneli afunika kumwalila.' \v 21 Ichi ndiye chamene mufunika kukamba mumitima mwanu: 'Nanga tizaziba bwanji utenga kapena Yehova akamba?'