1 line
279 B
Plaintext
1 line
279 B
Plaintext
\v 12 Aliyense amene achita mozikuza, osamvelela wansembe amene ayimilila kutumikila pamaso pa Yehovah Mulungu wanu, kapena posamvelela woweruza- uja mwamuna azamwalila; muzachosa choipa icho ku Israeli. \v 13 Banthu bonse bayenela kumvela na kuyopa, osachitanso kanthu mozikuza. |