nya-x-nyanja_deu_text_reg/16/03.txt

1 line
439 B
Plaintext

\v 3 Simuzadya mukate wopanda chotupisa; Masiku asanu ndi yabili muzadya mukate wopanda chotupisa, mukate wachisautso; chifukwa imwe munackokela mu malo mwa Egypto mwachangu. Chitani izi masiku yanu yonse ya umoyo wanu pakuti mukakubukile siku pamene munachokela mu malo ya Egypto. \v 4 Yisiti isaoneke pakati panu mumalo yanuonse masiku asanu na yabili ; kapena nyama yozipeleka nsembe mazulo pasiku yoyamba isakhale kufikila naku mawa.