nya-x-nyanja_deu_text_reg/09/21.txt

1 line
209 B
Plaintext

\v 21 Ninatenga uchimo wanu, mwana wa ng'ombe wamene munapanga, na kumushoka, kukamenya, na kukagaya kang'ono, mpaka kanankala monga doti. Ninataya doti yake mu mumana wamene unachokela pansi kuchoka kulupili.