nya-x-nyanja_deu_text_reg/09/07.txt

1 line
352 B
Plaintext

\v 7 Kumbukilani ndipo musaibale mwane imwe munasokoneza Yehova Mulungu wanu kukalipa muchipulu; kuchokela pa siku yamene imwe munachoka mu ziko ya Igputo mpaka imwe mubwela kuli yano malo, imwe mwankala osanvela mukusana na Yehova. \v 8 Napaja pa Horebu imwe munakalipisa Yehova ku ukali, ndipo Yehova anakalipa kwambili na imwe kuti akuonongeni imwe.