nya-x-nyanja_deu_text_reg/07/14.txt

1 line
325 B
Plaintext

\v 14 Muzadalisika kuchila bonse benangu banthu; Sikuzankala wamene azankala mwamuna alibe mwana kapena wosabala mukazi pakati pa imwe kapena pa zobeta zanu. \v 15 Yehova azachosapo pali imwe matenda; palibe pali yoipa matenda yaku Igputo yamene mwaziba yazaikidwa pali imwe, koma azayaika pali awo bonse bamene bazonda imwe.