nya-x-nyanja_deu_text_reg/05/15.txt

1 line
232 B
Plaintext

\v 15 Muzaitanila kunzelu kuli munali ba kapolo mu ziko ya Igputo, ndipo Yehova Mulungu wanu anakuchosani imwe kuchoka kuja na yampavu kwanja na kotambuluka kwanja. Ndiponso Yehova Mulungu wanu alamulila imwe kusunga siku ya sabata.