nya-x-nyanja_deu_text_reg/01/43.txt

1 line
313 B
Plaintext

\v 43 Ninakamba kuli imwe muli iyi njila, koma simunanvele. Munapanduka mosusana na malamulo ya Jehova; Munali ozikuza na kuukila ziko yapapili. \v 44 Koma ma Amori, bamene banankala pa ziko yapapili, banabwela mosusana naimwe na kukupilikishani monga nzimu, na kumenya imwe pansi mu Seir, kutali monga ku Hormah.