Sat Oct 02 2021 21:46:30 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
7545b6636c
commit
b94da0e7a2
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 20 Iwo ayenera kuuza akulu a mzinda wake kuti, 'Mwana wathuyu ndi wamakani ndiponso wopanduka; samvera mawu athu; ndi wosusuka ndi chidakwa. ' \v 21 Pamenepo amuna onse a mumzinda wake azim'ponya miyala kuti afe. kuti muchotse choipacho pakati panu. Aisraeli onse adzamva izi ndi kuchita mantha.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 22 Ngati munthu wachita tchimo loyenera imfa ndipo waphedwa, ndipo iwe nkumupachika pamtengo, \v 23 ndiye kuti mtembo wake suyenera kugona usiku wonse pamtengowo. M'malo mwake, umuike m'manda tsiku lomwelo; chifukwa aliyense wopachikidwa ndi wotembereredwa ndi Mulungu. Muzimvera lamuloli kuti musadetse dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti likhale cholowa chanu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 22
|
|
@ -315,6 +315,9 @@
|
|||
"21-13",
|
||||
"21-15",
|
||||
"21-18",
|
||||
"21-20",
|
||||
"21-22",
|
||||
"22-title",
|
||||
"33-01",
|
||||
"33-03",
|
||||
"33-05",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue