nya-x-nyanja_2sa_text_reg/21/07.txt

1 line
689 B
Plaintext

\v 7 Koma mfumu analekelela Mefiboshiti mwana mwamuna wa Jonathani mwana mwamuna wa Saulo, chifukwa chaku lumbila njazi kwa Yehova pakati kawo pakati ka Davide na Jonathani mwana mwamuna wa Saulo. \v 8 Koma mfumu anatenga bana bamuna babili ba Rizpa mwana mukazi wa Aia, bana bamuna bamene anabala kuli Saulo bana bamuna babili benze kuitaniwa Amoni na Mefiboshiti; Davide anatenga futi bana bamuna bali 5 ba Mirabi mwana mukazi wa Saulo, wamene anabala kuli Adrielo mwana mwamuna wa Bazilai mu Meholatiti. \v 9 Anabapasa mumanja mwama Gibyoniti. Bana ba pachika palupili pamenso ya Yehova, ndipo banafa bonse pamozi bali 7. Bana paiwa mu ntawi yokoloa, mukuyamba kwamasitu yoyamba balele.