nya-x-nyanja_2sa_text_reg/15/09.txt

1 line
315 B
Plaintext

\v 9 Pamene apo mfumu anakamba kuti, "Yenda mu mutendele." Pamene apo Abisalomu ananyamuka naku yenda ku Hebroni. \v 10 Koma chokonkapo Abisalomu anatuma bozanda muli zonse mutundu za Isilayeli. Kukamaba kuti, " Pamene chabe muzanvela chongo chalipenga, chokonkapo mukazmbe kuti Abisalomu ndiye mfumu mu Hebroni.'"