nya-x-nyanja_2sa_text_reg/14/30.txt

1 line
333 B
Plaintext

\v 30 Abisalomu anauza banchito bake kuti, "Onani munda wa Yowabu ulipafupi na wanga, elo sama yendako kuja. Yendani naku ushoka."Pamene apo banchito ba Abisalomu bana shoka minda. \v 31 Kuchoka apo Yowabu ananyamuka nakubwela kuli Abisalomu kunyumba yake, naku kamba kuli enve, "Nichani chamene banchito bako bashokela munda wanga?"