nya-x-nyanja_2sa_text_reg/08/15.txt

1 line
552 B
Plaintext

\v 15 Davidi analamulila pali Isilayeli, anapeleka chilungamo na chiyelo kuli bonse bantu. \v 16 Jowabu mwana mwamuna Zelia anali olamulila asilikali na Yohasafati mwana wa Ahiludi anali kalembela. \v 17 Zadoku mwana mwamuna wa Ahitubi na Ahimeleki anali asembe, na Seraya anali olemba. \v 18 Benaya mwana wa Jejoyada anali ayangan ila wa kereti na Peleti, ndipo bana ba Davidi banali nduna zabo. ***Mbili zakale Ageliki omasulila na ku masulila kwasopano zilina ivi mu mbili 18:17 kwamene akulu kulu omashila: koma zakale Ahaberi zosunga anali azembe.