nya-x-nyanja_2sa_text_reg/13/23.txt

1 line
403 B
Plaintext

\v 23 Chinafika kuti panapita zaka zokwanila zibili pamene Abisalomu anankala nabo bosebesenza kudyesela mbelele ku Baal Hazo, yamene ili pafupi na Eframu, Abisalomu anabaitana bonse bana bamuna ba mfumu kuti bamu tandalile kuja iye. \v 24 Abisalomu anayenda kuli mfumu naku kamba, "Onani manje, wanchito wanu alina bodyesela mbelele. Napapata, kuti mfumu na banchito bake bayende naine, wanchito wanu."