nya-x-nyanja_2sa_text_reg/13/10.txt

1 line
448 B
Plaintext

\v 10 Amoni anakmba kuli Tama kuti, "Leta vakudya muchipinda changa kuti tidye kuchokela mumanja yako. "Ndipo Tama anapeleka mukate wamene anabwela apanga, naku uleta muchipinda mwamubale wake Amoni. \v 11 Pamene analeta chakudya kuli enve, anamugwila iye nakukamba kuli enve kuti, "bwela ugone naine, mulonga wanga." \v 12 Anamuyanka iye kuti, "Iyayi, mubale wanga, usanipatikize sichifunika kuchitika mu Isilayeli. Usachite ichi chintu chonyansa!