nya-x-nyanja_2sa_text_reg/02/10.txt

1 line
261 B
Plaintext

\v 10 Isiboseti mwana wa Saulo, anali na zaka fote pamene ana yamba kulamulila Isilayeli, ndipo analamulila zaka zibili. Koma nyumba ya Yuda ina konka Davide. \v 11 Pa ntawi yamene Davidi anali mfumu ku Heberoni pa nyumba ya uda inali na seveni na myezi sikisi.