nya-x-nyanja_2sa_text_reg/14/23.txt

1 line
239 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 23 Pamene apo Yowabu ananyamuka kuyenda ku Gesha, naku leta Abisalomu kumubweza ku Yelusalemu. \v 24 Ba mfumu banakamba kuti, "Anga bwelele kunyumba yake, koma sanga one chinso changa." Pakunyumba kwake, koma sana one chinso cha mfumu.