Sun Oct 03 2021 11:26:46 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
cfdb89dabf
commit
d4a481b7d1
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 33 Ndipo Yehu anati, "Mponye pansi." Choncho anamuponyera pansi Yezebeli, ndipo magazi ake ena anawaza pa khoma ndi mahatchi ndipo Yehu anamupondaponda. \v 34 Yehu atalowa m'nyumba yachifumu, anayamba kudya ndi kumwa. Ndipo anati, Tawonanitu kwa mkazi wotembereredwa uyu, mumuike m'manda, chifukwa ndiye mwana wamkazi wa mfumu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 35 Anapita kukamuika maliro, koma osampeza koma chigaza, mapazi, ndi zikhatho za manja ake. \v 36 Choncho anabwerera ndi kukauza Yehu. Iye anati, "Awa ndi mawu a Yehova amene anayankhula kudzera mwa mtumiki wake Eliya Mtisibe, kuti, 'M'dziko la Yezreeli agalu adzadya mnofu wa Yezebeli, \v 37 ndipo thupi la Yezebeli lidzakhala ngati ndowe pamwamba pa minda ya m atdziko la Yezreeli, kotero kuti palibe amene adzanene kuti, “Uyu ndi Yezebeli.” '”
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 18 \v 19 \v 20 Pamenepo Yehu anasonkhanitsa anthu onse nanena nawo, Ahabu anatumikira Baala pang'ono, koma Yehu adzamtumikira kwambiri. Ndasiya nsembe, chifukwa ndili ndi nsembe yayikulu yoperekera Baala. Aliyense amene sabwera sadzakhala ndi moyo. " Koma Yehu anachita izi mwachinyengo kuti aphe olambira a Baala. Yehu anati, “Khazikitsani nthawi yopangira Baala.” Chifukwa chake adalengeza.
|
|
@ -161,8 +161,12 @@
|
|||
"09-27",
|
||||
"09-29",
|
||||
"09-30",
|
||||
"09-33",
|
||||
"09-35",
|
||||
"10-title",
|
||||
"10-01",
|
||||
"10-04",
|
||||
"10-06",
|
||||
"10-08",
|
||||
"10-10",
|
||||
"10-12",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue