Wed Sep 29 2021 12:37:23 GMT+0200 (Central Africa Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2021-09-29 12:37:23 +02:00
parent 1809aa0dfa
commit 64ef3f20b0
8 changed files with 9 additions and 30 deletions

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 24 Josiya anapilikisa baja banaliku kamba nabo kufa olo namizimu. Anapilikisa futi naba umfwiti, mafano, nazintu zonse zonyase zenzo oneka mu ziko ya Yuda namu Jerusalema, chakuti basimikizike mau ya lamulalo yanali yolembewa anapeza munyumba ya Yehova. \v 25 Kumbuyo kwa Josiya, kunalibe mfumu monga enve, anayangana kuli Yehova namutima wake onse, ,oyo wake onse, na mpavu zake zonse, anakonkeleza malamulo yonse ya Mose. Ndipo panalibe mfumu yina monga Josiya inayima pambuyo pake.
=======
\v 24 Josiah analesa bonse bamene benzeli ku kamba na okufa olo mizimu. Analesa futi atelafi na mafano, na voipa vonse vamene vinoneka mu malo ya Yuda na Yerusalemu, yanalembewa mu buku yamene Hilkiah wa nsembe anapeza mu nyumba ya Yehova. \v 25 Kumbuyo kwa Josiah, kunalibe mfumu monga eve, anayenda kwa Yahwe na mtima wake yonse, na mphamvu ake oinse, anakonkhya malamulo ya Mose yonse. Kapena kuzauka mfumu ina monga Josiah pasogolo pake.
>>>>>>> 59c7efc21795d7049b4a578b13805bd0f15561ea
\v 24 Josiya anapilikisa baja banaliku kamba nabo kufa olo namizimu. Anapilikisa futi naba umfwiti, mafano, nazintu zonse zonyase zenzo oneka mu ziko ya Yuda namu Jerusalema, chakuti basimikizike mau ya lamulalo yanali yolembewa anapeza munyumba ya Yehova. \v 25 Kumbuyo kwa Josiya, kunalibe mfumu monga enve, anayangana kuli Yehova namutima wake onse, ,oyo wake onse, na mpavu zake zonse, anakonkeleza malamulo yonse ya Mose. Ndipo panalibe mfumu yina monga Josiya inayima pambuyo pake.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 26 Koma, Yehova sanachinje kukalipa kwake koyofya, kwe anakalipila Yuda chifukwa cha vonse Manase anachita kulengesa kuti akalipe. \v 27 Yehova anakamba kuti, "Niza chosa futi na Yuda pamenso panga, mwenachosela Isialyeli, ndipo nizatenga uyu muzinda wenasanka, Jerusalema, na nyumba yamene ninakamba kuti, zina langa lizankalapo."
=======
\v 26 Koma, Yahwe sanakhuluke pa mkwiyo wake, wamene anashoka Yuda vamene Manasseh anacita. \v 27 Ndipo Yehwe anati, "Niachosa Yuda pamenso panga, monga nacosa Israyeli, nizataya mailo aya yamene nasankha, Yerusalemu, na nyumba yamene anakamba, ' Zina yanga izankhalamo"'
>>>>>>> 59c7efc21795d7049b4a578b13805bd0f15561ea
\v 26 Koma, Yehova sanachinje kukalipa kwake koyofya, kwe anakalipila Yuda chifukwa cha vonse Manase anachita kulengesa kuti akalipe. \v 27 Yehova anakamba kuti, "Niza chosa futi na Yuda pamenso panga, mwenachosela Isialyeli, ndipo nizatenga uyu muzinda wenasanka, Jerusalema, na nyumba yamene ninakamba kuti, zina langa lizankalapo."

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 28 Kuvintu vina vokumaniza Josiya, vonse ve anachita, sikuti nizo lembewa mu buku ya machitidwe ya mfumu za Yuda? \v 29 Mu masiku yake, Farao Necho, mfumu waku Iguputo, anayenda mukumenya nkondo na mfumu ya Asyria pa mumana wa Yufuletisi. mfumu Josiya anayenda mukumanya Necho ku Nkondo, ndipo Necho anamupaya ku Megido. \v 30 Kapolo wa Josiya anamunyala wokufa mungolo kuchokela ku Megido, nakumuleta ku Jerusalema, nakumushika mumanda yake. Bantu ba muziko banatenga Jehoahaz mwana wa Josiya, naku muzozeka, anamuyika kunkala mfumu mu malo mwa abambo ake.
=======
\v 28 Koma kukamba zankhani zina zokamba pa Josiah, zonse anacita, sizinalembewe mu buku yazocitika za mfumu ya Yuda? \v 29 Mu masiku aja, Farao Necho, mfumu ya Egypto, anayenda kumenyana na mfumu ya Assyria ku kamana ka Euphrates. Mfumu Josiah anayenda ku kumana na Necho mu nkhondo, na Necho anamupaya pa Megiddo. \v 30 Wanchito wa Josiah anamutenga pa gareta kucosa pa Magiddo, ku muleta ku Yerusalemu, anamuika mumanda yaje. Ndipo banthu ba mu malo anatenga mwana wake Jehoahaz mwana mwamuna wa Josiah, nakumuzoza eve, kupanga ankhale mfumu mu malo mwa atate bake.
>>>>>>> 59c7efc21795d7049b4a578b13805bd0f15561ea
\v 28 Koma kukamba zankhani zina zokamba pa Josiah, zonse anacita, sizinalembewe mu buku yazocitika za mfumu ya Yuda? \v 29 Mu masiku aja, Farao Necho, mfumu ya Egypto, anayenda kumenyana na mfumu ya Assyria ku kamana ka Euphrates. Mfumu Josiah anayenda ku kumana na Necho mu nkhondo, na Necho anamupaya pa Megiddo. \v 30 Wanchito wa Josiah anamutenga pa gareta kucosa pa Magiddo, ku muleta ku Yerusalemu, anamuika mumanda yaje. Ndipo banthu ba mu malo anatenga mwana wake Jehoahaz mwana mwamuna wa Josiah, nakumuzoza eve, kupanga ankhale mfumu mu malo mwa atate bake.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 31 Jehoahaz anali nazaka twenti sili pamene anayamba kulamulila, analamulia kwa myezi itatu mu Jerusalema, Bamai bake abanli Hamutal; anali mwana mukazi wa Jeremiya wake Libna. \v 32 Jehoabaz anachita vochimwa pa menso ya Yehova, monga vonse makolo bake banachita. \v 33 Farao Necho anamufaka mu unyolo ku Riblah mumalo ya Hamath, chakuti asalmulile mu Jerusalema. Necho analamulipilisa Yuda matalente asiliva ali handredi na tatende imozi ya golide.
=======
\v 31 Jehoahaz anali wa zaka twenti - fili pamene anayamba ku lamumulira, analamulira miyezi fili cabe mu Yerusalemu. Amai bake bake zina yabo yezeli Hamutal; banali mwana mukazi wa Jeremiah waku Lubinah. \v 32 Jehoahaz anacita coipa ku mnso kwa Yahwe monga makolo bake bonse banacitila. Farao Necho anamuika mu macheni ku Riblah mu malo ya Hamath, Kuti nasalamulile mu Yerusalemu. \v 33 Ndipo Necho anamupasa mtenga Yuda makhumi khumi yama talente yasilira talente imozi ya golide.
>>>>>>> 59c7efc21795d7049b4a578b13805bd0f15561ea
\v 31 Jehoahaz anali wa zaka twenti - fili pamene anayamba ku lamumulira, analamulira miyezi fili cabe mu Yerusalemu. Amai bake bake zina yabo yezeli Hamutal; banali mwana mukazi wa Jeremiah waku Lubinah. \v 32 Jehoahaz anacita coipa ku mnso kwa Yahwe monga makolo bake bonse banacitila. Farao Necho anamuika mu macheni ku Riblah mu malo ya Hamath, Kuti nasalamulile mu Yerusalemu. \v 33 Ndipo Necho anamupasa mtenga Yuda makhumi khumi yama talente yasilira talente imozi ya golide.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 34 Farao Necho anayika Ehakim mwana wa Josiya mfumu pa malo ya abambo ake, nakumupasa zina la Jehoiakim. koma anapeleka Jehoahoaz ku Iguputo, ndipo Jehoahaz anafela kwamene. \v 35 Jehoaikim analipila siliva na golide kuli Farao. chakuti akwanise ve analikufuna Farao, Jehoiakim analipilila malo sonko naku kakamiza mwamuna alionse pa bantu bamumalo kumulipila siliva na golide kulingana na zintu zawo.
=======
\v 34 Farao Necho anapanga mwana mwamuna wa Josiah Eliakim mfumu mumalo mwa atate bake Josiah, anachinja zina yake kunkhala Jehoiakim. Koma anatenga Jehoahaz kucoka ku Egypto, na Jehoahaz anafela kuja. \v 35 Jehoiakim analipila siliva na golide kuli Farao. Ndipo kwanilisa kufuna kwa Farao, Jehoikim kusonkhesa malo kubakakamiza pa anthu , mumalo aba kuti apeleke kwaiye siliva na golide monga mwa kufuna kwake.
>>>>>>> 59c7efc21795d7049b4a578b13805bd0f15561ea
\v 34 Farao Necho anapanga mwana mwamuna wa Josiah Eliakim mfumu mumalo mwa atate bake Josiah, anachinja zina yake kunkhala Jehoiakim. Koma anatenga Jehoahaz kucoka ku Egypto, na Jehoahaz anafela kuja. \v 35 Jehoiakim analipila siliva na golide kuli Farao. Ndipo kwanilisa kufuna kwa Farao, Jehoikim kusonkhesa malo kubakakamiza pa anthu , mumalo aba kuti apeleke kwaiye siliva na golide monga mwa kufuna kwake.

View File

@ -1,5 +1 @@
<<<<<<< HEAD
\v 36 Jehoiakim anali nazaka twenti-faive pamene anayamba klamulila, analamulila kwa zaka ileveni mu Jerusalema. Zina yaba mai bake inali Zebida; anali mwana wa Pedaia waku Rumah. \v 37 Jehoiakim anachita zochimwa pa menso ya Yehova, monga zonse makolo bake banachita.
=======
\v 36 Jehoiakim anali wazaka twenti -0 faivi pamene anayamba kulamulira, analamulira zaka ileveni mu Yerusalemu. Amai bake zina yabo yeze Zebidah; banali mwana mukazi wa Pedaiad waku Rumah. \v 37 Jehoiakim anacita zoipa pa menso ya Yahwe, monga anacita makolo bake.
>>>>>>> 59c7efc21795d7049b4a578b13805bd0f15561ea
\v 36 Jehoiakim anali nazaka twenti-faive pamene anayamba klamulila, analamulila kwa zaka ileveni mu Jerusalema. Zina yaba mai bake inali Zebida; anali mwana wa Pedaia waku Rumah. \v 37 Jehoiakim anachita zochimwa pa menso ya Yehova, monga zonse makolo bake banachita.

1
24/title.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
Mutu 24

View File

@ -278,6 +278,8 @@
"21-10",
"21-13",
"22-title",
"23-36",
"24-title",
"24-01",
"24-03",
"24-05",