1 line
450 B
Plaintext
1 line
450 B
Plaintext
\v 3 Pamene Mfumukazi yaku Seba inaona nzelu za Solomoni na nyumba yaufumu yamene anamanga, \v 4 vakudya pa tebulo yake, ponkala pa banchito bake, nchito za banchito bake na vovala vawo, omupelekela chiko na vovala vawo, na nsembe zoshoka zamene anapeleka ku [[Akatswiri ena amanena kuti mawu akuti “nsembe zopsereza zimene anapereka” m’njira ina anganene kuti, “chitunda chimene anakwerapo”.]] nyumba ya Yehova, munalibe na mpepo muli eve. |