2 lines
402 B
Plaintext
2 lines
402 B
Plaintext
\v 22 Mwa njira imeneyi, Yehova anapulumutsa Hezekiya ndi anthu okhala mu Yerusalemu m'manja mwa Sanakeribu, mfumu ya Asuri, ndi m'manja mwa ena onse, ndipo anawapatsa mpumulo mbali zonse.
|
|
\v 23 Ambiri anali kubweretsa zopereka kwa Yehova ku Yerusalemu, ndi mphatso zamtengo wapatali kwa Hezekiya mfumu ya Yuda, kotero kuti anayamba kukwezeka pamaso pa anthu a mitundu yonse kuyambira nthawi imeneyo. |