nya-x-nyanja_2ch_text_reg/32/18.txt

1 line
282 B
Plaintext

\v 18 Adafuwula mchilankhulo cha Ayuda kwa anthu aku Yerusalemu omwe anali pakhomalo, kuti awawopsyeze ndi kuwasokoneza, kuti alande mzindawo. \v 19 Adalankhula za Mulungu waku Yerusalemu monga adalankhulira za milungu ya anthu ena padziko lapansi, omwe ndi ntchito ya manja aanthu.