nya-x-nyanja_2ch_text_reg/25/25.txt

1 line
252 B
Plaintext

\v 25 Amaziya mwana wa Yowasi mfumu ya Yuda anankala na moyo zaka kumi na zisanu pambuyo pa infa ya Yoasi mwana wa Yehoahazi mfumu ya Israeli. \v 26 Nkhani zina zokuza Amaziya, zoyambilila ai zomalizila, zinalembewa mubuku ya mafumu ya Yuda na Israeli.