nya-x-nyanja_2ch_text_reg/25/18.txt

1 line
451 B
Plaintext

\v 18 Koma Yoasi mfumu ya Israeli anatumiza amitenga kuli Amaziya mfumu ya Yuda, kuti, "Munga wa ku Lebano unatumiza utenga kuli mkunguza waku Lebano, kuti, Upase mwana wanga ankale mkazi, koma amtchile Chilombo cha ku Lebanoni chinausha na kupondaponda chisamba chaminga, \v 19 Wa kamba, 'Onani nakanta Edomu,' na mtima wako. Tenga kuzi nvela muku pambana kwako, koma unkale kunyumba, chifukwa ungazifake mukubvutika na kugwa iwe pamodzi na Yuda? ”