2 lines
364 B
Plaintext
2 lines
364 B
Plaintext
\v 14 Manje chinabwela, Amaziya anabwelela kuchokela kokakanta Aedomu, analeta tu mulungu twa bantu ba ku Seiri, na kutuimika kunkala tu mulungu twake. Anatu
|
|
gwadila na kutushokela lubani. \v 15 Mwaicho ukali wa Yehova unayakila Amaziya. Anamtumizila mneneli wamene anakamba, "Chifukwa cha chani mwafuna tumilungu twa bantu bamene sanapulumuse bantu mumabja yabo?" |