nya-x-nyanja_2ch_text_reg/25/14.txt

2 lines
364 B
Plaintext

\v 14 Manje chinabwela, Amaziya anabwelela kuchokela kokakanta Aedomu, analeta tu mulungu twa bantu ba ku Seiri, na kutuimika kunkala tu mulungu twake. Anatu
gwadila na kutushokela lubani. \v 15 Mwaicho ukali wa Yehova unayakila Amaziya. Anamtumizila mneneli wamene anakamba, "Chifukwa cha chani mwafuna tumilungu twa bantu bamene sanapulumuse bantu mumabja yabo?"