nya-x-nyanja_2ch_text_reg/25/01.txt

1 line
226 B
Plaintext

\c 25 \v 1 Amaziya anali na zaka 25 pamene anayamba ku lamulila; analamulila na zaka 29 mu Yerusalemu. Amayi bake zina yabo inali Yehoadana, wa ku Yerusalemu. \v 2 Anachita zoyenera pamenso pa Yehova, koma osati na mtima onse.