nya-x-nyanja_2ch_text_reg/24/23.txt

1 line
421 B
Plaintext

\v 23 Kosilizila chaka, gulu yankondo inabwela kumenyana na Yowasi. Bana bwela kuli Yuda na ku Yerusalemu; anapaya batsogoleli bonse bantu na zofunka zawo zonse anazitumiza kuli mfumu ya ku Damasiko. \v 24 Ngakale kuti gulu yankondo inabwela na asilikali yochepa, Yehova anabapasa gulu yankondo ikulu kwambili, chifukwa Bayuda banasiya Yehova, Mulungu wa makolo wabo. Munjila iyi Ŵaaramu bana leta kuweluza kuli Yowashi.