nya-x-nyanja_2ch_text_reg/24/15.txt

1 line
236 B
Plaintext

\v 15 Yehoyada anakula ndipo anali na zaka zambili, ndipo anafa; anali na zaka 130 pamene anafa. \v 16 Bana mushika mumanda mu Mzinda wa Davide pakati pa mafumu, chifukwa anachita zabwino mu Israeli, kwa Mulungu na ku nyumba ya Mulungu.