nya-x-nyanja_2ch_text_reg/23/18.txt

1 line
358 B
Plaintext

\v 18 Yehoyada anaika oyanganila nyumba ya Yehova mosamalila wansembe, Alevi, wamene Davide anabapasa nyumba ya Yehova, kuti apeleke nsembe zopseleza kuli Yehova, monga mwalembewa mucilamulo cha Mose, ndi kusekelela na kuimba monga Davide analangiza. \v 19 Yehoyada anaika bolonda pazipata za nyumba ya Yehova kuti aliyense wadoti mu njila iliyonse asangene.