1 line
340 B
Plaintext
1 line
340 B
Plaintext
\v 14 Ndipo wansembe Yehoyada anachosa bosogolela mazana akuyanganila nkondo, na kukamba kuli beve, ''Muchoseni pakati pa magulu; aliyense wamene azamukonka, lekani apaiwe na lupanga.'' Popeza wansembe anakamba, Usamupaile munyumba ya Yehova.' \v 15 Anamugwila pamene anali kungen pachipata cha matchi * cha munyumba ya mfumu, na ku mupaya. |