nya-x-nyanja_2ch_text_reg/23/14.txt

1 line
340 B
Plaintext

\v 14 Ndipo wansembe Yehoyada anachosa bosogolela mazana akuyanganila nkondo, na kukamba kuli beve, ''Muchoseni pakati pa magulu; aliyense wamene azamukonka, lekani apaiwe na lupanga.'' Popeza wansembe anakamba, Usamupaile munyumba ya Yehova.' \v 15 Anamugwila pamene anali kungen pachipata cha matchi * cha munyumba ya mfumu, na ku mupaya.