1 line
367 B
Plaintext
1 line
367 B
Plaintext
\v 6 Musa vomeleze kuti aliyense angene munyumba ya Yehova, kuchoselako bansembe na Alevi bamene bamtumikila. Banga ngene chifukwa nibo zipeleka. Koma bantu bena bonse bafunikila kumvela malamulo ya Yahweh. \v 7 Alevi azungulukila mfumu paliponse, muntu aliyense atenga zida zake mumanja. Aliyense ongena munyumba apaiwe. Muzinkala na mfumu ikangena kapena ikachoka." |