nya-x-nyanja_2ch_text_reg/23/01.txt

1 line
609 B
Plaintext

\c 23 \v 1 Muchaka cha 7, Yehoida anaonesa mphamvu zake na kuchita chipangano naba sogoleli ba magulu ya bantu muma gulu 100, Azariya mwana wa Yerohamu, Ismayeli mwana wa Yehohanani, Azariya mwana wa Obedi, Maseya mwana wa Adaya, na Elisafati mwana wa Zikiri. \v 2 Banayendayenda mu Yuda na kusonkana Alevi kuchokela mumizinda zonse za Yuda, na basogoleli ba mabanja ya Israyeli, ndipo banabwela ku Yerusalemu. \v 3 Zonse msonkano zina panga pangano na mfumu munyumba ya Mulungu; Yehoyada anababuza kuti, “Onani, mwana wa mfumu azalamulila monga mwamene Yehova anakambila pali bana naba bazikulu ba Davide.