1 line
480 B
Plaintext
1 line
480 B
Plaintext
\c 14 \v 1 Abiya anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo anamuika m’manda mu Mzinda wa Davide. Asa mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake. M’masiku ake dziko linali labata zaka khumi. \v 2 Asa anachita zabwino ndi zoyenera pamaso pa Yehova Mulungu wake, \v 3 pakuti anachotsa maguwa ansembe achilendo ndi misanje. Anaphwanya zipilala zamiyala ndi kugwetsa mizati ya Asera. \v 4 Iye anauza Yuda kuti afunefune Yehova Mulungu wa makolo awo, ndi kutsatira chilamulo + ndi malamulo. |