1 line
450 B
Plaintext
1 line
450 B
Plaintext
\v 10 Koma ife, Yehova ndiye Mulungu wathu, + ndipo sitinamusiye. Tili ndi ansembe, zidzukulu za Aroni, otumikira Yehova, ndi Alevi amene amagwira ntchito yawo. \v 11 M’mawa ndi madzulo onse amafukizira Yehova nsembe zopsereza ndi zofukiza zonunkhira bwino. Iwo amakonzanso mkate woonekera patebulo loyera. azisamaliranso choikapo nyale chagolide, ndi nyali zake, aziyaka madzulo onse. Timasunga malamulo a Yehova Mulungu wathu, koma inu mwamusiya. |