nya-x-nyanja_2ch_text_reg/13/08.txt

1 line
538 B
Plaintext
Raw Permalink Blame History

This file contains ambiguous Unicode characters

This file contains Unicode characters that might be confused with other characters. If you think that this is intentional, you can safely ignore this warning. Use the Escape button to reveal them.

\v 8 Chotero mukuganizira zolimbana ndi ufumu wa Yehova umene uli mmanja mwa ana a Davide, chifukwa ndinu gulu lankhondo lalikulu, ndipo muli ndi ana a ngombe agolide amene Yerobiamu anawapanga kuti akhale milungu yanu. \v 9 Koma simunapitikitsa ansembe a Yehova, zidzukulu za Aroni, ndi Alevi, ndi kudzipangira ansembe inu, monga amachitira anthu a mmaiko ena? Aliyense amene wabwera kudzatumikira monga wansembe ndi kupereka nsembe ngombe yaingono yamphongo ndi nkhosa zamphongo 7, adzakhala wansembe wa imene si milungu.