1 line
538 B
Plaintext
1 line
538 B
Plaintext
\v 8 Chotero mukuganizira zolimbana ndi ufumu wa Yehova umene uli m’manja mwa ana a Davide, chifukwa ndinu gulu lankhondo lalikulu, ndipo muli ndi ana a ng’ombe agolide amene Yerobiamu anawapanga kuti akhale milungu yanu. \v 9 Koma simunapitikitsa ansembe a Yehova, zidzukulu za Aroni, ndi Alevi, ndi kudzipangira ansembe inu, monga amachitira anthu a m’maiko ena? Aliyense amene wabwera kudzatumikira monga wansembe ndi kupereka nsembe ng’ombe yaing’ono yamphongo ndi nkhosa zamphongo 7, adzakhala wansembe wa imene si milungu. |