1 line
343 B
Plaintext
1 line
343 B
Plaintext
\v 15 Nkhani zina zokhudza Rehobowamu, zoyamba ndi zomalizira, zinalembedwa m’mabuku a mneneri Semaya ndi Ido wamasomphenya, m’mabuku a mibadwo ya makolo awo ndi za nkhondo za nthawi zonse pakati pa Rehobowamu ndi Yerobiamu? \v 16 Nagona Rehabiamu ndi makolo ace, naikidwa m'mudzi wa Davide; Abiya mwana wake anakhala mfumu m’malo mwake. |