1 line
387 B
Plaintext
1 line
387 B
Plaintext
\v 9 Choncho Sisaki mfumu ya Iguputo inabwera kudzamenyana ndi Yerusalemu n’kutenga chuma cha m’nyumba ya Yehova, ndi chuma cha m’nyumba ya mfumu. Iye anachotsa chirichonse; anatenganso zishango zagolide zimene Solomo anapanga. \v 10 Mfumu Rehobowamu inapanga zishango zamkuwa m’malo mwake, n’kuzipereka m’manja mwa akuluakulu a asilikali olondera zitseko za nyumba ya mfumu. |