1 line
327 B
Plaintext
1 line
327 B
Plaintext
\v 5 Tsopano mneneri Semaya anabwera kwa Rehobowamu ndi kwa atsogoleri a Yuda amene anasonkhana ku Yerusalemu chifukwa cha Sisaki. Semaya anati kwa iwo, Atero Yehova, Inu mwandisiya ine, chotero inenso ndakuperekani m’dzanja la Sisaki. \v 6 Pamenepo akalonga a Israyeli ndi mfumu anadzichepetsa, nati, Yehova ndiye wolungama. |