1 line
406 B
Plaintext
1 line
406 B
Plaintext
\v 2 M’chaka chachisanu cha Mfumu Rehobowamu, + Sisaki mfumu ya Iguputo inabwera kudzamenyana ndi Yerusalemu chifukwa anthuwo sanalakwire Yehova. \v 3 Anadza ndi magareta mazana khumi ndi awiri, ndi apakavalo zikwi makumi asanu ndi limodzi. Ankhondo osawerengeka anadza naye ku Igupto: Alibiya, Suki, ndi Akusi. \v 4 Analanda mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri ya Yuda n’kupita ku Yerusalemu. |