1 line
372 B
Plaintext
1 line
372 B
Plaintext
\v 10 Anyamata amene anakulira pamodzi ndi Rehobowamu anamuuza kuti: “Ukauze anthu amene anakuuzani kuti Solomo atate wanu analemetsa goli lawo, koma inu mulipeputse. ukawauze kuti, ‘Chala changa chaching’ono n’chachikulu kuposa chiuno cha atate wanga, \v 11 ndipo tsopano, ngakhale kuti bambo anga anakusenzetsani goli lolemera, ine ndidzakukwapulani ndi zikoti." |